10 ensinamentos do Novo Testamento
O Novo Testamento reúne os ensinamentos centrais da fé cristã. Nele estão registrados os ensinamentos de Jesus, a mensagem dos apóstolos e as orientações dadas às primeiras comunidades cristãs. Esses textos apresentam princípios espirituais, morais e práticos que orientam a vida cristã.
Neste artigo, você vai conhecer 10 ensinamentos do Novo Testamento, apresentados em forma de lista com versículos bíblicos que resumem a essência da mensagem cristã.
1. Amar a Deus acima de tudo
Yesu anayankha kuti, "Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse ndi moyo wako wonse ndi nzeru zako zonse.
2. Amar o próximo como a si mesmo
Ndipo lachiwiri ndi lofanana nalo: ‘Konda mnansi wako monga iwe mwini.’
3. Perdoar aqueles que erram contra você
Mukomerane mtima ndi kuchitirana chifundo wina ndi mnzake. Khululukiranani wina ndi mnzake, monga momwe Mulungu anakukhululukirani mwa Khristu.
4. Buscar primeiro o Reino de Deus
Koma muyambe mwafuna ufumu wake ndi chilungamo chake ndipo zinthu zonsezi zidzapatsidwa kwa inu.
5. Viver pela fé
Ife timakhala mwachikhulupiriro, osati mwa zooneka ndi maso.
6. Praticar a humildade
Musachite kalikonse ndi mtima odzikonda chabe kapena odzitukumula chabe. Koma khalani odzichepetsa ndipo aliyense aziona mnzake ngati womuposa iyeyo.
7. Servir ao próximo
Pakuti ngakhale Mwana wa Munthu sanabwere kudzatumikiridwa, koma kudzatumikira, ndi kupereka moyo wake kuti ukhale dipo la anthu ambiri."
8. Permanecer na Palavra de Deus
Ana a Abrahamu
Kwa Ayuda amene anamukhulupirira, Yesu anati, "Ngati inu mutsatira chiphunzitso changa, ndithu ndinu ophunzira anga.
9. Viver em santidade
Koma monga amene anakuyitanani ndi woyera, inunso khalani oyera mtima mʼmakhalidwe anu wonse. Pakuti, kwalembedwa kuti, "Khalani oyera mtima, chifukwa Ine ndine Woyera."
10. Anunciar o evangelho
Chifukwa chake, pitani kaphunzitseni anthu a mitundu yonse, ndi kuwabatiza mʼdzina la Atate ndi la Mwana ndi la Mzimu Woyera,
Conclusão
Os ensinamentos do Novo Testamento revelam princípios fundamentais da fé cristã, como amor, fé, perdão, humildade e compromisso com a mensagem do evangelho.
Esses princípios orientam a vida espiritual e mostram o caminho ensinado por Jesus e pelos apóstolos.
Se este conteúdo ajudou você a conhecer os principais ensinamentos do Novo Testamento, compartilhe este artigo para que mais pessoas também possam aprender com a Palavra de Deus.