Pular para o conteúdo
Publicidade
Voltar para início

Bíblia Hoje

5 Ago

Gideoni anayankha, "Koma mbuye wanga, ngati Yehova ali nafedi, nʼchifukwa chiyani zonsezi zationekera? Nanga ntchito zake zodabwitsa zimene makolo athu anatiwuza pamene anati, ‘Yehova anatitulutsa ku dziko la Igupto,’ zili kuti? Koma tsopano Yehova watitaya ndi kutipereka mʼmanja mwa Amidiyani."

Juízes 6:13

Zimenezi zikukondweretseni kwambiri, ngakhale tsopano, kwa kanthawi kochepa, mukumva zowawa mʼmayesero osiyanasiyana. Mayeserowa abwera nʼcholinga chakuti chikhulupiriro chanu, chimene ndi chamtengo woposa wa golide, amene amawonongeka ngakhale amayengedwa ndi moto, chitsimikizike kuti ndi chenicheni. Pamenepo ndiye mudzalandire mayamiko, ulemerero ndi ulemu pamene Yesu Khristu adzaoneka.

1 Pedro 1:6,7

Provérbios 5 adverte sobre os perigos da imoralidade, encorajando a fidelidade no casamento e a prudência nas ações.

Provérbios 5

O Salmo 67 é uma oração pedindo a bênção de Deus sobre as nações, para que todos O conheçam e louvem.

Salmos 67
Publicidade

Em Destaque

Ver tudo

Últimos Artigos

Ver tudo

Deus quer falar com você!

Receba a Palavra do Senhor no seu WhatsApp.