10 versículos para fortalecer os laços familiares
A Bíblia enfatiza a importância da família e nos ensina como viver em harmonia com nossos entes queridos. Neste artigo, vamos explorar 10 versículos bíblicos que podem fortalecer os laços familiares e nos ajudar a refletir sobre o papel da família à luz da Palavra de Deus.
Versículos
1. Provérbios 22:6
Mwana muzimuphunzitsa njira yake,
ndipo akadzakalamba sadzachokamo.
2. Salmos 127:3
Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,
ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
3. Colossenses 3:20
Inu ana, mverani makolo anu mu zonse pakuti izi zimakondweretsa Ambuye.
4. Êxodo 20:12
"Lemekeza abambo ako ndi amayi ako kuti ukhale ndi moyo wautali mʼdziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.
5. Provérbios 1:8
Malangizo kuti Asunge Nzeru
Malangizo kwa Achinyamata
Mwana wanga, mvera malangizo a abambo ako
ndipo usakane mawu okuwongolera a amayi ako.
6. Josué 24:15
Koma ngati kutumikira Yehova kukuyipirani, sankhani lero amene mudzamutumikire, kapena milungu imene makolo anu ankayitumikira kutsidya kwa mtsinje wa Yufurate, kapena milungu ya Aamori, amene mukukhala mʼdziko lawo. Koma ine ndi banja langa, tidzatumikira Yehova."
7. Deuteronômio 6:6-7
Malamulo amene ndakupatsani lero ayenera kukhala mu mtima mwanu. Muziwaphunzitsa mwachangu kwa ana anu. Muzikamba za malamulowa pamene muli mʼnyumba zanu, pamene mukuyenda mʼnjira, pamene mukugona ndi pamene mukudzuka.
8. Salmo 128:3
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka
mʼkati mwa nyumba yako;
ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi
kuzungulira tebulo lako.
9. Provérbios 15:20
Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake,
koma mwana wopusa amanyoza amayi ake.
10. Efésios 5:25
Inu amuna, kondani akazi anu monga momwe Khristu anakondera mpingo nadzipereka yekha mʼmalo mwa mpingowo
Esses versículos sobre a família nos lembram da importância de honrar, amar e cuidar uns dos outros. Medite neles e viva em harmonia, de acordo com os ensinamentos de Deus.
Compartilhe este artigo para inspirar outras famílias a serem fortalecidas pela Palavra de Deus.
Deus abençoe!