Pular para o conteúdo
Publicidade

10 versículos sobre esperar o tempo de Deus

Por Bíblia Online

Esperar o tempo de Deus é um princípio presente em toda a Bíblia. As Escrituras ensinam que Deus age no momento certo e que a confiança nele deve permanecer mesmo quando não há respostas imediatas.

Neste artigo, você encontrará 10 versículos sobre esperar o tempo de Deus para fortalecer sua fé e lembrar das promessas bíblicas.

1. Eclesiastes 3:1

Chilichonse Chili ndi Nthawi

Chinthu chilichonse chili ndi nthawi yake,

ndi nyengo yake yomwe anayika Mulungu:

2. Salmos 27:14

Dikirani pa Yehova;

khalani anyonga ndipo limbani mtima

nimudikire Yehova.

3. Isaías 40:31

koma iwo amene amakhulupirira Yehova

adzalandira mphamvu zatsopano.

Adzawuluka ngati chiwombankhanga;

adzathamanga koma sadzalefuka,

adzayenda koma sadzatopa konse.

4. Salmos 37:7

Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa;

usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo,

pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa.

5. Lamentações 3:25-26

Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,

kwa munthu amene amafunafuna Iyeyo;

nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha

Yehova modekha.

6. Habacuque 2:3

Pakuti masomphenyawa akudikira nthawi yake;

masomphenyawa akunena zamʼtsogolo

ndipo sizidzalephera kuchitika.

Ngakhale achedwe kukwaniritsidwa, uwayembekezere;

zidzachitika ndithu ndipo sadzachedwa.

7. Salmos 130:5

Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera,

ndipo ndimakhulupirira mawu ake.

8. Romanos 8:25

Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.

9. Miquéias 7:7

Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,

ndikudikira Mulungu Mpulumutsi wanga;

Mulungu wanga adzamvetsera.

10. Gálatas 6:9

Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.

Conclusão

Os versículos sobre esperar o tempo de Deus reforçam a importância da confiança, da paciência e da perseverança na vida cristã.

Se este conteúdo foi útil para você, compartilhe com outras pessoas para que mais vidas sejam fortalecidas pela Palavra de Deus.

Josiane de Souza Campos
1 pessoa deu Amém