10 versículos sobre esperar o tempo de Deus
Esperar o tempo de Deus é um princípio presente em toda a Bíblia. As Escrituras ensinam que Deus age no momento certo e que a confiança nele deve permanecer mesmo quando não há respostas imediatas.
Neste artigo, você encontrará 10 versículos sobre esperar o tempo de Deus para fortalecer sua fé e lembrar das promessas bíblicas.
1. Eclesiastes 3:1
Chilichonse Chili ndi Nthawi
Chinthu chilichonse chili ndi nthawi yake,
ndi nyengo yake yomwe anayika Mulungu:
2. Salmos 27:14
Dikirani pa Yehova;
khalani anyonga ndipo limbani mtima
nimudikire Yehova.
3. Isaías 40:31
koma iwo amene amakhulupirira Yehova
adzalandira mphamvu zatsopano.
Adzawuluka ngati chiwombankhanga;
adzathamanga koma sadzalefuka,
adzayenda koma sadzatopa konse.
4. Salmos 37:7
Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa;
usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo,
pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa.
5. Lamentações 3:25-26
Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,
kwa munthu amene amafunafuna Iyeyo;
nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha
Yehova modekha.
6. Habacuque 2:3
Pakuti masomphenyawa akudikira nthawi yake;
masomphenyawa akunena zamʼtsogolo
ndipo sizidzalephera kuchitika.
Ngakhale achedwe kukwaniritsidwa, uwayembekezere;
zidzachitika ndithu ndipo sadzachedwa.
7. Salmos 130:5
Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera,
ndipo ndimakhulupirira mawu ake.
8. Romanos 8:25
Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.
9. Miquéias 7:7
Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,
ndikudikira Mulungu Mpulumutsi wanga;
Mulungu wanga adzamvetsera.
10. Gálatas 6:9
Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.
Conclusão
Os versículos sobre esperar o tempo de Deus reforçam a importância da confiança, da paciência e da perseverança na vida cristã.
Se este conteúdo foi útil para você, compartilhe com outras pessoas para que mais vidas sejam fortalecidas pela Palavra de Deus.