10 versículos sobre esperar o tempo de Deus
Esperar o tempo de Deus é um princípio presente em toda a Bíblia. As Escrituras ensinam que Deus age no momento certo e que a confiança nele deve permanecer mesmo quando não há respostas imediatas.
Neste artigo, você encontrará 10 versículos sobre esperar o tempo de Deus para fortalecer sua fé e lembrar das promessas bíblicas.
1. Eclesiastes 3:1
Chilichonse Chili ndi Nthawi
Chinthu chilichonse chili ndi nthawi yake,
ndi nyengo yake yomwe anayika Mulungu:
2. Salmos 27:14
Dikirani pa Yehova;
khalani anyonga ndipo limbani mtima
nimudikire Yehova.
3. Isaías 40:31
koma iwo amene amakhulupirira Yehova
adzalandira mphamvu zatsopano.
Adzawuluka ngati chiwombankhanga;
adzathamanga koma sadzalefuka,
adzayenda koma sadzatopa konse.
4. Salmos 37:7
Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa;
usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo,
pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa.
5. Lamentações 3:25-26
Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,
kwa munthu amene amafunafuna Iyeyo;
nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha
Yehova modekha.
6. Habacuque 2:3
Pakuti masomphenyawa akudikira nthawi yake;
masomphenyawa akunena zamʼtsogolo
ndipo sizidzalephera kuchitika.
Ngakhale achedwe kukwaniritsidwa, uwayembekezere;
zidzachitika ndithu ndipo sadzachedwa.
7. Salmos 130:5
Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera,
ndipo ndimakhulupirira mawu ake.
8. Romanos 8:25
Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.
9. Miquéias 7:7
Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,
ndikudikira Mulungu Mpulumutsi wanga;
Mulungu wanga adzamvetsera.
10. Gálatas 6:9
Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.
Conclusão
Os versículos sobre esperar o tempo de Deus reforçam a importância da confiança, da paciência e da perseverança na vida cristã.
Se este conteúdo foi útil para você, compartilhe com outras pessoas para que mais vidas sejam fortalecidas pela Palavra de Deus.
Este artigo te tocou? Faça uma oração!
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.