A fé vem pelo ouvir
A fé vem pelo ouvir, e o ouvir pela Palavra de Cristo. Quando a Palavra é proclamada, a fé nasce nos corações. Ouvir a Deus é o primeiro passo para crer e seguir.
A fé vem pelo ouvir
A fé vem pelo ouvir, e o ouvir pela Palavra de Cristo. Quem ouve a Palavra crê e obtém a salvação eterna.
Chindhu ichi ni kwa wonjhe, pakuti balibe kusiyana kwa Ayahudi ni anyiawo osati ayahudi, Mbuye wa wonjhe ni mmojhi, naye wali ni ubwino kupunda kwa wandhu ampembha. Yalembedwa chimwechi mmalembo ya Mnungu, "Mundhu waliyonjhe uyo siwapembhe kwa ulamuli wa jhina la Ambuye siwaomboledwe."
Chipano sampembhe bwanji iye samkhulupilila? Nianyiiwo, samkhulupilile bwanji ngati sadavela nghani zake? Nisavele bwanji ngati palibe mundhu olalikila? Ni wandhu salalikile bwanji ngati sadapelekedwe? Ngati umo yalembedwa mmalembo ya Mnungu, "Chindhu chokwada kupunda kujha kwa wajha alalikila Uthenga Wabwino!" Nambho asati wonjhe adaulandila Uthenga Wabwino. Nde ndande Isaya wadakamba, "Mbuye ni yani uyo wadakhulupilila uthenga wathu?" Chimwecho, chikhulupi chichokana ni kuvela Uthenga Wabwino, ni uthenga umeneo uchokana ni mawu la Kilisito.
Nikonda kujhiwa chindhu chimojhipe kuchoka kwanu. Bwanji, mdalandila Mzimu wa Mnungu ndande ya kuchita ngati umo lifunila thauko, kapina ndande ya kuuvela ni kuukhulupilila Uthenga wa Bwino?
Chimchijha namwenjho, wandhu yawo asatia Ayahudi mudauvela Uthenga wa uzene, uthenga uwo wakupelekelani uomboli. Mudamkhulupilila Kilisito, ni kukuikani chizindikilo kulangiza kuti wake kwa kukupachani Mzimu yujha Mnungu wadatikambila kuti siwatupache. Mzimu umenewo ndeuwo wachita tiyapate yonjhe yayo wadatikambila Mnungu kwa wandhu wake, chindhu ichi chitilangiza kuti Mnungu siwaombole wandhu wake onjhe. Ife tiutamande ulemelelo wake.
"Zene nikukambilani, mundhu waliyonjhe uyo wavela mawu yanga ni kwaakhulupilila Amnungu yawo anituma, ali ni umoyo wa muyaya. Sialamulidwa muyaya, nambho wachoka kunyifa ni kulowa kuumoyo.
Zene nikukambilani, ndhawi ikujha ni chipano ilipo, yapo omwalila savele mvekelo wa Mwana wa Amnungu, ni anyiyao savele mvekelo saakhale ni umoyo.
Palibe mundhu uyo wakhoza kujha kwanga, ngati siwadaghuzidwe ni Atate yao anituma, nane sinimuhyuche mundhu mneyo siku lo thela. Yalembedwa mvikalakala va alosi, ‘Wandhu wonjhe sayaluzidwe ni Amnungu.’ Waliyonjhe uyo waavela Atate ni kujhiyaluza kwa iwo, wakujha kwanga. Palibe uyo waonapo Atate, nambho uyo wachoka kwa Amnungu, mmeyo nde uyo waona Atate. Nikukambilani zene, uyo wakhulupilila wali ni umoyo wa muyaya.
Ouvir e obedecer
Felizes os que ouvem a Palavra de Deus e a praticam. Quem tem ouvidos ouça o que o Espírito diz.
Nambho Yesu wadayangha, "Ali ni mwawi kupunda yawo avela mawu ya Mnungu ni kuyachata."
Mchate icho mkambidwa!"
Chimwecho wadaakambila, "Pitani kujhiko lonjhe la panjhi, mkalalikile wandhu wonjhe Uthenga Wabwino.
Yakwanila kwaanyiiwo yajha wadakamba mlosi Isaya,
‘Kuvela simvele, nambho simujhiwa.
Kupenya simujhipenya, nambho simuona.
Pakuti mitima ya wandhu yawa ni yolimba,
ayacheka makutu yawo,
athimila maso yawo.
Popande chimwecho, adakaona kwa maso yawo,
adakavela kwa makutu yawo,
adakajhiwa kwa njelu zawo,
adakanichata,
nane nidakaalamicha.’ "
"Nambho anyiimwe muli ni mwawi, pakuti maso yanu yapenya ni makutu yanu yavela.
Vindhu ivo vimchita mundhu siwadavomelezeka pa kumlambila Mnungu
Ndiipo Yesu wadalitana gulu la wandu lijha, wadalikambila, "Mnivechele ni mvanenavo!