5 atitudes cristãs para viver melhor em família
Ah… família! Todos nós temos aqueles parentes que somos mais próximos e outros mais distantes. Cada um com sua razão, mas que muitas vezes causam desavenças ou situações que enfraquecem os laços familiares. Mas como mudar isso?\\\\ Aplicando princípios cristãos.
Na Bíblia conseguimos ver algumas atitudes que nos podem servir de exemplo e por isso, separamos aqui 5 versículos bíblicos que podem te ajudar a melhorar os seus laços familiares.
Lista de atitudes:
1. 1 Coríntios 13:4-7
Chikondi nʼcholeza mtima, chikondi nʼchokoma mtima, chilibe nsanje, sichidzikuza, sichidzitamandira. Chikondi chilibe mwano, sichodzikonda, sichipsa mtima msanga, sichisunga mangawa. Chikondi sichikondwera ndi zoyipa koma chimakondwera ndi choonadi. Chimatchinjiriza nthawi zonse, chimakhulupirika nthawi zonse, chimakhala ndi chiyembekezo nthawi zonse, chimapirira nthawi zonse.
2. Efésios 4:32
Mukomerane mtima ndi kuchitirana chifundo wina ndi mnzake. Khululukiranani wina ndi mnzake, monga momwe Mulungu anakukhululukirani mwa Khristu.
3. Efésios 5:33
Chomwecho, aliyense mwa inu akuyenera kukonda mkazi wake monga adzikondera iye mwini, ndipo mkazi akuyenera kulemekeza mwamuna wake.
4. Colossenses 3:12-13
Choncho, ngati anthu osankhidwa ndi Mulungu, oyera mtima ndi okondedwa kwambiri, muvale chifundo, kukoma mtima, kudzichepetsa, kufatsa ndi kupirira. Mulezerane mtima ndipo muzikhululukirana ngati wina ali ndi chifukwa ndi mnzake. Muzikhululukirana monga Ambuye anakhululukira inu.
5. Mateus 18:20
Pakuti pamene awiri kapena atatu asonkhana pamodzi mʼdzina langa, Ine ndili nawo pomwepo."
Algum desses versículos te ajudou com alguma situação que tenha vivido? Ou conhece alguém que está passando por algum problema com a família? Então compartilhe esses versículos para ajudar a fortalecer os laços familiares por meio de princípios cristãos.
Deus abençoe!