Pular para o conteúdo
Publicidade

10 versículos que mostram o amor de Deus

Por Bíblia Online

1. João 3:16

"Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha.

O versículo mais conhecido da Bíblia revela o maior ato de amor: o sacrifício de Jesus por nós.

2. Romanos 5:8

Koma Mulungu anaonetsa chikondi chake kwa ife chifukwa pamene tinali ochimwabe, Khristu anatifera.

O amor de Deus não depende do nosso merecimento. Ele nos amou primeiro, mesmo em nossa imperfeição.

3. Lamentações 3:22-23

Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,

ndi chifundo chake ndi chosatha.

Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;

kukhulupirika kwanu nʼkwakukulu.

O amor de Deus se renova todos os dias com misericórdia e fidelidade.

4. Salmo 103:11

Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,

koteronso chikondi chake nʼchachikulu kwa iwo amene amamuopa;

O salmista nos lembra da imensidão do amor divino: algo que está acima da compreensão humana.

5. 1 João 4:9-10

Mmene Mulungu anaonetsera chikondi chake pakati pathu ndi umu: Iye anatumiza Mwana wake mmodzi yekha ku dziko lapansi kuti mwa Iyeyo tikhale ndi moyo. Chikondi ndi ichi: osati kuti ife ndife amene tinamukonda Mulungu, koma kuti Iyeyo ndiye amene anatikonda ndipo anatumiza Mwana wake kuti akhale nsembe yopepesera machimo athu.

Um amor que age, salva e transforma. Deus é o iniciador de todo verdadeiro amor.

6. Salmo 136:26

Yamikani Mulungu wakumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Um refrão que ecoa por todo o Salmo 136 e reforça a verdade imutável: o amor de Deus é eterno.

7. Sofonias 3:17

Yehova Mulungu wako ali pakati pako,

ali ndi mphamvu yopulumutsa.

Adzakondwera kwambiri mwa iwe,

adzakukhalitsa chete ndi chikondi chake,

adzayimba mokondwera chifukwa cha iwe."

Um versículo poderoso que mostra o prazer que Deus tem em amar seus filhos.

8. Isaías 54:10

Ngakhale mapiri atagwedezeka

ndi zitunda kusunthidwa,

koma chikondi changa chosasinthika pa iwe sichidzatha.

Pangano langa lamtendere silidzasintha,"

akutero Yehova amene amakuchitira chifundo.

Mesmo que tudo mude, o amor de Deus permanece firme.

9. Jeremias 31:3

Ine ndinawaonekera ndili chapatali ndipo ndinati,

"Ine ndakukondani ndi chikondi chopanda malire.

Nʼchifukwa chake ndipitiriza kukukondani.

Deus nos atrai com seu amor eterno, um amor que precede o tempo e permanece em toda estação.

10. Efésios 2:4-5

Koma chifukwa cha chikondi chake chachikulu pa ife, Mulungu amene ndi olemera mʼchifundo, anatipanga kukhala amoyo ndi Khristu ngakhale pamene ife tinali akufa mu zolakwa zathu. Koma tinapulumutsidwa mwachisomo.

Um amor que ressuscita e dá nova vida, mesmo quando estamos espiritualmente mortos.

Estes versículos revelam o coração de Deus: amoroso, fiel, constante. Não importa o momento que você esteja vivendo, a Palavra nos garante que o amor do Senhor é real, ativo e disponível. Releia essas passagens, ore com elas, compartilhe com quem precisa de consolo. Que esse amor transforme seu coração e fortaleça sua fé diariamente.

Se este artigo te abençoou, compartilhe com seus amigos e familiares!

Seja o primeiro