10 versículos bíblicos para enviar no ano novo
O Ano Novo é um momento de reflexão, renovação e esperança. Compartilhar versículos bíblicos com amigos e familiares é uma maneira especial de abençoar e encorajar aqueles que amamos.
Confira 10 versículos inspiradores para enviar no Ano Novo:
1. Jeremias 29:11
Pakuti Ine ndikudziwa zimene ndinakukonzerani," akutero Yehova, "ndimalingalira zabwino zokhazokha za inu osati zoyipa, ayi. Ndimalingalira zinthu zokupatsani chiyembekezo chenicheni pa za mʼtsogolo.
Esse versículo é um lembrete de que Deus tem um plano perfeito para o novo ano.
2. Filipenses 3:13-14
Abale, sindidziyesera ndekha kuti ndachipeza kale chimenechi. Koma chinthu chimodzi chimene ndimachita, nʼkuyiwala zamʼmbuyo ndi kuthamangira molimbika zinthu zimene zili mʼtsogolo mwanga. Ndikuthamangira kokathera mpikisanowo kuti ndikalandire mphotho imeneyi kumwamba, imene Mulungu anandiyitanira mwa Khristu Yesu.
Uma motivação para deixar o passado para trás e seguir adiante.
3. Provérbios 16:3
Pereka ntchito zako zonse mʼmanja mwa Yehova,
ndipo zolinga zako zidzachitikadi.
Encoraje alguém a dedicar seus planos a Deus.
4. Isaías 40:31
koma iwo amene amakhulupirira Yehova
adzalandira mphamvu zatsopano.
Adzawuluka ngati chiwombankhanga;
adzathamanga koma sadzalefuka,
adzayenda koma sadzatopa konse.
Uma mensagem de força e renovação para o novo ciclo.
5. Salmos 37:5
Pereka njira yako kwa Yehova;
dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:
Um convite para confiar plenamente em Deus no Ano Novo.
6. Lamentações 3:22-23
Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,
ndi chifundo chake ndi chosatha.
Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;
kukhulupirika kwanu nʼkwakukulu.
Reforce a ideia de que o novo ano traz novas bênçãos.
7. Deuteronômio 31:8
Yehova mwini ndiye akukutsogolerani ndipo adzakhala nanu. Sadzakusiyani kapena kukutayani. Usachite mantha ndiponso usataye mtima."
Uma mensagem de coragem para os desafios futuros.
8. Romanos 8:28
Oposa Agonjetsi
Ndipo ife tikudziwa kuti zinthu zonse zimathandizana kuwachitira ubwino amene amakonda Mulungu, amene anayitanidwa monga mwa cholinga chake.
Um lembrete de que Deus está no controle de tudo.
9. Salmos 65:11
Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka,
ndipo ngolo zanu zimasefukira ndi zinthu zochuluka.
Ideal para começar o ano com gratidão pela bondade de Deus.
10. 2 Coríntios 5:17
Nʼchifukwa chake, ngati munthu aliyense ali mwa Khristu, ndi wolengedwa kwatsopano; zinthu zakale zapita taonani, zakhala zatsopano.
Perfeito para enviar com desejos de renovação.
Envie esses versículos e ajude a espalhar a Palavra de Deus!