10 versículos sobre fé para fortalecer a confiança em Deus
Existem momentos de fraqueza, onde nós abalamos nossa fé. Ou nos vemos nos questionando sobre a mesma. Mas faz parte, somos humanos e é natural que desvios aconteçam, desde que lembremos que Deus está sempre de braços abertos para nos receber e acolher.
Sabendo disso, é fato que a fé é o grande alicerce da vida cristã e para te ajudar a se reconectar ou fortalecer sua confiança em Deus, preparamos neste artigo 10 versículos poderosos que fortalecerão sua confiança em nosso Senhor.
Lista de versículos:
1. Hebreus 11:1
Tsopano chikhulupiriro ndi kusakayika konse pa zinthu zimene tikuziyembekeza, ndi kutsimikiza kuti zinthu zimene sitiziona zilipo ndithu.
2. Marcos 11:24
Nʼchifukwa chake ndikukuwuzani kuti chilichonse chimene mupempha mʼpemphero, khulupirirani kuti mwalandira, ndipo chidzakhala chanu.
3. 2 Coríntios 5:7
Ife timakhala mwachikhulupiriro, osati mwa zooneka ndi maso.
4. Romanos 10:17
Motero, chikhulupiriro chimabwera pamene timva uthenga ndipo uthenga umamveka kuchokera ku mawu a Khristu.
5. Salmos 37:5
Pereka njira yako kwa Yehova;
dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:
6. Tiago 1:6
Koma pamene mupempha, muyenera kukhulupirira osakayika, chifukwa amene amakayika ali ngati mafunde pa nyanja amene amawinduka nakankhika ndi mphepo.
7. Mateus 21:22
Ngati mukhulupirira, mudzalandira chilichonse chimene muchipempha mʼpemphero."
8. João 20:29
Kenaka Yesu anamuwuza kuti, "Kodi wakhulupirira chifukwa wandiona Ine? Ndi odala amene amakhulupirira ngakhale asanaone."
9. Efésios 2:8
Pakuti mwapulumutsidwa mwachisomo, kudzera mʼchikhulupiriro ndipo izi sizochokera mwa inu eni, koma ndi mphatso ya Mulungu,
10. Gálatas 2:20
Ndinapachikidwa pa mtanda pamodzi ndi Khristu, kotero kuti sindinenso amene ndili ndi moyo, koma ndi Khristu amene ali ndi moyo mwa ine. Moyo umene ndili nawo tsopano mʼthupi lino, ndi moyo mwachikhulupiriro mwa Mwana wa Mulungu, amene anandikonda nadzipereka yekha chifukwa cha ine.
Compartilhe esses versículos sobre fé e ajude a fortalecer a confiança dos seus irmãos no Senhor. Que este artigo também tenha sido ponte para que você engrandeça ainda mais sua fé em Deus.
Deus abençoe!