Publicidade

1 Coríntios 15

55 "Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti?

Iwe imfa, ululu wako uli kuti?"

56 Ululu wa imfa ndi tchimo, ndipo mphamvu ya tchimo ndi lamulo. 57 Koma tiyamike Mulungu amene amatipambanitsa mwa Ambuye athu Yesu Khristu.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-