Pular para o conteúdo
Publicidade

1 Crônicas 16

34 Yamikani Yehova, pakuti Iye ndi wabwino;

chikondi chake chikhala mpaka muyaya.

35 Fuwulani kuti, "Tipulumutseni, Inu Mulungu wa chipulumutso chathu,

mutisonkhanitse ndipo mutipulumutse kwa anthu a mitundu ina,

kuti tiyamike dzina lanu loyera,

kuti tikutamandeni."

36 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli,

kuyambira muyaya mpaka muyaya.

Ndipo anthu onse anati, "Ameni" ndipo "Tikutamandani Yehova."

Veja também