12 Chuma ndi ulemu zimachokera kwa Inu;
Inu ndinu wolamulira zinthu zonse.
Mʼdzanja lanu muli nyonga ndi mphamvu,
kukweza ndi kupereka nyonga kwa onse.
12 Chuma ndi ulemu zimachokera kwa Inu;
Inu ndinu wolamulira zinthu zonse.
Mʼdzanja lanu muli nyonga ndi mphamvu,
kukweza ndi kupereka nyonga kwa onse.