24 Pakuti,
"Anthu onse ali ngati udzu,
ndipo ulemerero wawo uli ngati duwa la kuthengo.
Udzu umafota ndipo duwa limathothoka,
25 koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya."
Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu.
24 Pakuti,
"Anthu onse ali ngati udzu,
ndipo ulemerero wawo uli ngati duwa la kuthengo.
Udzu umafota ndipo duwa limathothoka,
25 koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya."
Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu.