Pular para o conteúdo
Publicidade

1 Pedro 5

5 Momwemonso, inu anyamata gonjerani amene ndi akulu. Inu nonse mukhale odzichepetsa kuti mutumikirane, chifukwa,

"Mulungu amatsutsana nawo odzikuza,

koma amapereka chisomo kwa odzichepetsa."

6 Choncho, mudzichepetse pamaso pa Mulungu wamphamvu, kuti pa nthawi yake adzakukwezeni. 7 Tayani pa Iye nkhawa zanu zonse chifukwa ndiye amakusamalani.

Veja também