Pular para o conteúdo
Publicidade

1 MAFUMU 2

19 Batiseba atapita kwa Mfumu Solomoni kukayankhula naye mʼmalo mwa Adoniya, mfumu inanyamuka kukumana naye, ndipo inaweramira amayi akewo, kenaka inakhala pa mpando wake waufumu. Iye anayitanitsa mpando wina kuti amayi ake akhalepo ndipo anakhala pansi ku dzanja lake lamanja.

20 Amayi akewo anati, "Ndikufuna ndikupempheni kanthu kakangʼono. Chonde musandikanize."

Mfumu inayankha kuti, "Pemphani amayi, ine sindikukanizani."

Veja também