26 Mayi amene mwana wake anali moyo anagwidwa ndi chisoni chifukwa cha mwana wakeyo ndipo anawuza mfumu kuti, "Chonde mbuye wanga, mupatseni mnzangayu mwana wamoyoyu! Musamuphe!"
Koma winayo anati, "Ayi, asandipatse ine kapena iwe. Muduleni pakati!"
26 Mayi amene mwana wake anali moyo anagwidwa ndi chisoni chifukwa cha mwana wakeyo ndipo anawuza mfumu kuti, "Chonde mbuye wanga, mupatseni mnzangayu mwana wamoyoyu! Musamuphe!"
Koma winayo anati, "Ayi, asandipatse ine kapena iwe. Muduleni pakati!"