22 Koma Samueli anayankha kuti,
"Kodi Yehova amakondwera ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zina
kapena kumvera mawu a ake?
Taona, kumvera ndi kwabwino kuposa nsembe,
ndipo kutchera khutu ndi kwabwino kuposa kupereka mafuta a nkhosa.
22 Koma Samueli anayankha kuti,
"Kodi Yehova amakondwera ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zina
kapena kumvera mawu a ake?
Taona, kumvera ndi kwabwino kuposa nsembe,
ndipo kutchera khutu ndi kwabwino kuposa kupereka mafuta a nkhosa.