23 Pakuti kuwukira kuli ngati tchimo lowombeza,
ndipo kukhala nkhutukumve kuli ngati tchimo lopembedza mafano.
Chifukwa mwakana mawu a Yehova.
Iyenso wakukana kuti iweyo ukhale mfumu."
23 Pakuti kuwukira kuli ngati tchimo lowombeza,
ndipo kukhala nkhutukumve kuli ngati tchimo lopembedza mafano.
Chifukwa mwakana mawu a Yehova.
Iyenso wakukana kuti iweyo ukhale mfumu."