16 Mosakayikira, chinsinsi cha chikhulupiriro chathu chachikulu:
Khristu anaonekera ali ndi thupi la munthu,
Mzimu anamuchitira umboni,
angelo anamuona,
analalikidwa pakati pa mitundu yonse,
dziko lapansi linamukhulupirira,
anatengedwa kupita kumwamba mwa ulemerero.