17 Akulu ampingo amene amayangʼanira bwino zochitika za mu mpingo, ndi oyenera ulemu wowirikiza, makamaka amene ntchito yawo ndi kulalikira ndi kuphunzitsa. 18 Pakuti Mawu a Mulungu amati, "Musamange ngʼombe pakamwa pamene ikupuntha tirigu," ndi "Wantchito ngoyenera kulandira malipiro ake."
Publicidade
Publicidade