6 Koma kulemekeza Mulungu kuli ndi phindu lalikulu. 7 Pakuti sitinabweretse kanthu mʼdziko lapansi, ndipo sitingatengenso kanthu pochoka mʼdziko lapansi. 8 Koma ngati tili ndi chakudya ndi zovala, zimenezi zitikwanire.
Publicidade
1 TIMOTEYO 6
Estes versículos te tocaram? Ore agora!
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.