Pular para o conteúdo
Publicidade

2 Pedro 2

Aphunzitsi Onyenga

1 Koma panalinso aneneri onama pakati pa Aisraeli, monga padzakhalanso aphunzitsi onyenga pakati panu. Iwo adzalowetsa mwamseri ziphunzitso zonama ndi zowononga, nadzakana Ambuye amene anawawombola, ndipo motero adzadziyitanira okha chiwonongeko mwadzidzidzi.

Veja também

2 Pedro
Ver todos os capítulos de 2 Pedro