Pular para o conteúdo
Publicidade

2 MAFUMU 22

Buku la Malamulo Lipezeka

1 Yosiya anakhala mfumu ali ndi zaka zisanu ndi zitatu ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 31. Amayi ake anali Yedida mwana wa Adaiya wochokera ku Bozikati.

Veja também