16 Elisa anati kwa mayiyo, "Nthawi ngati yomwe ino chaka chamawa, udzakhala utanyamula mwana wamwamuna mʼmanja mwako."
Mayiyo anatsutsa zimenezi nanena kuti, "Ayi mbuye wanga. Inu munthu wa Mulungu, musanamize mdzakazi wanu!"
16 Elisa anati kwa mayiyo, "Nthawi ngati yomwe ino chaka chamawa, udzakhala utanyamula mwana wamwamuna mʼmanja mwako."
Mayiyo anatsutsa zimenezi nanena kuti, "Ayi mbuye wanga. Inu munthu wa Mulungu, musanamize mdzakazi wanu!"