Pular para o conteúdo
Publicidade

2 Timóteo 1

Kumvera Paulo ndi Uthenga Wabwino

6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja. 7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga.

Veja também

2 Timóteo
Ver todos os capítulos de 2 Timóteo