Lipenga Lachisanu ndi Chiwiri
15 Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati,
"Ufumu wa dziko lapansi uli
mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja,
ndipo adzalamulira mpaka muyaya."
15 Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati,
"Ufumu wa dziko lapansi uli
mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja,
ndipo adzalamulira mpaka muyaya."