Pular para o conteúdo
Publicidade

Apocalipse 12

9 Chinjoka chachikulu chija chinagwetsedwa pansi. Ichocho ndiye njoka yakalekale ija yotchedwa Mdierekezi kapena Satana, amene amasocheretsa anthu a pa dziko lonse lapansi. Chinaponyedwa pa dziko la pansi pamodzi ndi angelo ake.

10 Kenaka ndinamva mawu ofuwula kumwamba akunena kuti,

"Tsopano chipulumutso, mphamvu,

ufumu wa Mulungu wathu

ndi ulamuliro wa Khristu wake zabwera.

Pakuti woneneza abale athu uja,

amene amangokhalira kuwaneneza pamaso pa Mulungu usana ndi usiku,

wagwetsedwa pansi.

Veja também