Publicidade

Apocalipse 7

16 Iwowa sadzamvanso njala,

sadzamvanso ludzu,

dzuwa kapena kutentha kulikonse

sikudzawawotcha.

17 Pakuti Mwana Wankhosa amene ali pakati pa mpando waufumu

adzakhala mʼbusa wawo.

Iye adzawatsogolera ku akasupe a madzi amoyo.

Ndipo Mulungu adzawapukuta misozi yonse mʼmaso mwawo.’ "

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-