4 Korneliyo anamuyangʼanitsitsa mngeloyo mwa mantha. Iye anafunsa kuti, "Nʼchiyani kodi Ambuye?"
Mngelo anayankha kuti, "Mapemphero ako ndi zachifundo zako zafika pamaso pa Mulungu ngati chikumbutso.
4 Korneliyo anamuyangʼanitsitsa mngeloyo mwa mantha. Iye anafunsa kuti, "Nʼchiyani kodi Ambuye?"
Mngelo anayankha kuti, "Mapemphero ako ndi zachifundo zako zafika pamaso pa Mulungu ngati chikumbutso.