Pular para o conteúdo
Publicidade

Atos 10

4 Korneliyo anamuyangʼanitsitsa mngeloyo mwa mantha. Iye anafunsa kuti, "Nʼchiyani kodi Ambuye?"

Mngelo anayankha kuti, "Mapemphero ako ndi zachifundo zako zafika pamaso pa Mulungu ngati chikumbutso.

Veja também