Paulo Asiyana ndi Barnaba
36 Patapita masiku ena Paulo anati kwa Barnaba, "Tiyeni tibwerere kuti tikaone abale ku mizinda yonse imene tinalalika Mawu a Ambuye ndipo tikaone mmene akuchitira." 41 Iye anadutsa ku Siriya ndi ku Kilikiya kupita akulimbikitsa mipingo.