30 Iye anawatulutsa kunja ndipo anawafunsa kuti, "Amuna inu, ndichite chiyani kuti ndipulumuke?"
31 Iwo anayankha kuti, "Khulupirira Ambuye Yesu ndipo udzapulumuka, iwe ndi a mʼbanja lako."
30 Iye anawatulutsa kunja ndipo anawafunsa kuti, "Amuna inu, ndichite chiyani kuti ndipulumuke?"
31 Iwo anayankha kuti, "Khulupirira Ambuye Yesu ndipo udzapulumuka, iwe ndi a mʼbanja lako."