Pular para o conteúdo
Publicidade

Atos 6

Asankha Atumiki Asanu ndi Awiri

1 Mʼmasiku amenewo pamene chiwerengero cha ophunzira chinkachuluka, Ayuda a Chihelene pakati pawo anadandaula chifukwa cha Ayuda a Chihebri chifukwa amasiye awo samawagawira chakudya cha tsiku ndi tsiku.

6 Iwo anapereka anthuwa kwa atumwi amene anawapempherera ndi kuwasanjika manja.

Veja também