Pular para o conteúdo
Publicidade

Atos 6

9 Panauka mtsutso kuchokera kwa anthu a ku Kurene ndi a ku Alekisandriya komanso a ku dera la Silisiya ndi Asiya, otchedwa a Sunagoge ya Mfulu. Anthu amenewa anayamba kutsutsana ndi Stefano.

11 Iwo ananyengerera anthu ena mwamseri kuti anene kuti, "Ife tinamva Stefano akuchitira chipongwe Mose ndiponso Mulungu."

Veja também