59 Akumugenda miyala, Stefano anapemphera kuti, "Ambuye Yesu, landirani mzimu wanga." 60 Ndipo anagwada pansi nafuwula mwamphamvu kuti, "Ambuye musawawerengere tchimoli." Atanena mawu amenewa anamwalira.
59 Akumugenda miyala, Stefano anapemphera kuti, "Ambuye Yesu, landirani mzimu wanga." 60 Ndipo anagwada pansi nafuwula mwamphamvu kuti, "Ambuye musawawerengere tchimoli." Atanena mawu amenewa anamwalira.