2 Pa nthawi imeneyi, ine Danieli ndinalira kwa masabata atatu. 3 Sindinadye chakudya chokoma; nyama ndi vinyo sizinakhudze milomo yanga ndi pangʼono pomwe; ndipo sindinadzole mafuta aliwonse mpaka patatha masabata atatu.
2 Pa nthawi imeneyi, ine Danieli ndinalira kwa masabata atatu. 3 Sindinadye chakudya chokoma; nyama ndi vinyo sizinakhudze milomo yanga ndi pangʼono pomwe; ndipo sindinadzole mafuta aliwonse mpaka patatha masabata atatu.