Publicidade

Eclesiastes 1

4 Mibado imabwera ndipo mibado imapita,

koma dziko lapansi limakhalapobe nthawi zonse.

5 Dzuwa limatuluka ndipo dzuwa limalowa

ndipo limapita mwamsanga kumene limatulukira.

6 Mphepo imawombera cha kummwera

ndi kukhotera cha kumpoto;

imawomba mozungulirazungulira,

kumangobwererabwerera komwe yachokera.

7 Mitsinje yonse imakathira ku nyanja,

koma nyanjayo sidzaza;

kumene madziwo amachokera,

amabwereranso komweko.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-