Pular para o conteúdo
Publicidade

MLALIKI 1

4 Mibado imabwera ndipo mibado imapita,

koma dziko lapansi limakhalapobe nthawi zonse.

5 Dzuwa limatuluka ndipo dzuwa limalowa

ndipo limapita mwamsanga kumene limatulukira.

6 Mphepo imawombera cha kummwera

ndi kukhotera cha kumpoto;

imawomba mozungulirazungulira,

kumangobwererabwerera komwe yachokera.

7 Mitsinje yonse imakathira ku nyanja,

koma nyanjayo sidzaza;

kumene madziwo amachokera,

amabwereranso komweko.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também