Pular para o conteúdo
Publicidade

MLALIKI 11

Kuponya Chakudya pa Madzi

1 Ponya chakudya chako pa madzi,

udzachipezanso patapita masiku ambiri.

2 Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu,

pakuti sudziwa ndi tsoka lanji limene likubwera pa dziko.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também