11 Iwo ankayimba motamanda ndi mothokoza Yehova nyimbo iyi:
"Yehova ndi wabwino;
chikondi chake pa Israeli ndi chamuyaya."
Ndipo anthu onse ankafuwula kwambiri kumutamanda Yehova, chifukwa maziko a Nyumba ya Yehova anali kumangidwa.
11 Iwo ankayimba motamanda ndi mothokoza Yehova nyimbo iyi:
"Yehova ndi wabwino;
chikondi chake pa Israeli ndi chamuyaya."
Ndipo anthu onse ankafuwula kwambiri kumutamanda Yehova, chifukwa maziko a Nyumba ya Yehova anali kumangidwa.