22 Pamenepo Farao analamulira anthu ake onse kuti, "Mwana wamwamuna aliyense akabadwa, mukamuponye mu mtsinje wa Nailo, koma wamkazi mulekeni akhale ndi moyo."
22 Pamenepo Farao analamulira anthu ake onse kuti, "Mwana wamwamuna aliyense akabadwa, mukamuponye mu mtsinje wa Nailo, koma wamkazi mulekeni akhale ndi moyo."