2 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
ndiye chipulumutso changa.
Iye ndiye Mulungu wanga, ndipo ndidzamutamanda,
Mulungu wa makolo anga, ine ndidzamukweza.
2 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
ndiye chipulumutso changa.
Iye ndiye Mulungu wanga, ndipo ndidzamutamanda,
Mulungu wa makolo anga, ine ndidzamukweza.