Pular para o conteúdo
Publicidade

Êxodo 16

2 Mʼchipululumo gulu lonse linadandaulira Mose ndi Aaroni 3 kuti, "Kukanakhala bwino Yehova akanatiphera mʼdziko la Igupto! Kumeneko timadya nyama ndi buledi mpaka kukhuta, koma inu mwabwera nafe ku chipululu kudzapha mpingo wonsewu ndi njala!"

Veja também