Pular para o conteúdo
Publicidade

Êxodo 5

Mose Akumana ndi Farao

1 Zitachitika izi, Mose ndi Aaroni anapita kwa Farao ndipo anati, "Yehova Mulungu wa Israeli akuti, Aloleni anthu anga apite, kuti akachite chikondwerero cha Ine mʼchipululu.’ "

Veja também