Pular para o conteúdo
Publicidade

AGALATIYA 3

16 Malonjezo awa anaperekedwa kwa Abrahamu ndi kwa mbewu yake. Malemba sakunena kuti, "kwa mbewu zake," kutanthauza anthu ambiri, koma, "kwa mbewu yako," kutanthauza munthu mmodzi, amene ndi Khristu.

Veja também