Publicidade

Gênesis 1

Chiyambi cha Chilengedwe

1 Pachiyambi Mulungu analenga kumwamba ndi dziko lapansi. 2 Dziko lapansi linali losakonzedwa ndi lopanda kanthu. Mdima wandiweyani unakuta nyanja ndipo Mzimu wa Mulungu unkayendayenda pamwamba pa madziwo.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-