18 Ndipo Melikizedeki mfumu ya ku Salemu anabweretsa buledi ndi vinyo. Iyeyu anali wansembe wa Mulungu Wammwambamwamba,
20 Ndipo adalitsike Mulungu Wammwambamwamba
amene anapereka adani ako mʼdzanja lako."
Ndipo Abramu anamupatsa iye chakhumi cha zonse anali nazo.