17 Atangowatulutsa, mmodzi wa angelowo anati, "Thawani kuti mudzipulumutse, musachewuke, musayime pena paliponse mʼchigwamo! Thawirani ku mapiri kuopa kuti mungawonongeke!"
17 Atangowatulutsa, mmodzi wa angelowo anati, "Thawani kuti mudzipulumutse, musachewuke, musayime pena paliponse mʼchigwamo! Thawirani ku mapiri kuopa kuti mungawonongeke!"