Pular para o conteúdo
Publicidade

Gênesis 2

16 Ndipo Yehova Mulungu analamula munthu uja kuti, "Uzidya zipatso za mu mtengo wina uliwonse mʼmundamu; 17 koma usadye zipatso za mu mtengo wodziwitsa chabwino ndi choyipa, popeza ukadzadya za mu mtengowu udzafa ndithu."

Veja também