Pular para o conteúdo
Publicidade

Gênesis 28

20 Pamenepo Yakobo analumbira kwa Yehova nati, "Ngati inu Mulungu mukhala ndi ine, kundiyangʼanira pa ulendo wangawu ndi kundipatsa chakudya ndi chovala; 22 ndipo mwala uwu ndawuyimikawu udzakhala Nyumba ya Mulungu. Ine ndidzakupatsani chakhumi cha zinthu zonse zimene mudzandipatse."

Veja também