19 Kuti upeze chakudya udzayenera
kukhetsa thukuta,
mpaka utabwerera ku nthaka
pakuti unachokera kumeneko;
pakuti ndiwe fumbi
ku fumbi komweko udzabwerera."
19 Kuti upeze chakudya udzayenera
kukhetsa thukuta,
mpaka utabwerera ku nthaka
pakuti unachokera kumeneko;
pakuti ndiwe fumbi
ku fumbi komweko udzabwerera."