25 Adamu anagonanso malo amodzi ndi mkazi wake, ndipo anabereka mwana wamwamuna namutcha Seti, kutanthauza kuti, "Mulungu wandipatsa mwana wina mʼmalo mwa Abele, popeza Kaini anamupha."
25 Adamu anagonanso malo amodzi ndi mkazi wake, ndipo anabereka mwana wamwamuna namutcha Seti, kutanthauza kuti, "Mulungu wandipatsa mwana wina mʼmalo mwa Abele, popeza Kaini anamupha."